1 Samueli 27:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Davide ananyamuka, naoloka pamodzi ndi anthu mazana asanu ndi limodzi amene anali naye, nafika kwa Akisi mwana wa Maoki, mfumu ya ku Gati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Davide ananyamuka, naoloka pamodzi ndi anthu mazana asanu ndi limodzi amene anali naye, nafika kwa Akisi mwana wa Maoki, mfumu ya ku Gati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Davide adanyamuka, ndipo pamodzi ndi ankhondo 600 amene anali naye, adapita kwa Akisi, mwana wa Maoki, mfumu ya ku Gati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho Davide ndi anthu 600 amene anali nawo anachoka napita kwa Akisi mwana wa Maoki mfumu ya ku Gati. Onani mutuwo |