1 Samueli 1:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo womnyodolayo anamputa kwakukulu, kuti amuwawitse mtima, popeza Yehova anatseka mimba yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo womnyodolayo anamputa kwakukulu, kuti amuwawitse mtima, popeza Yehova anatseka mimba yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono chifukwa choti Chauta sadampatse ana, mkazi mnzake uja ankangomnyodola ndi kumpeputsa, kuti amkwiyitse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tsono popeza Yehova sanamupatse Hana ana, mkazi mnzakeyo ankamuyamba dala ndi cholinga chomukwiyitsa. Onani mutuwo |