1 Samueli 1:5 - Buku Lopatulika5 koma anapatsa Hana magawo awiri, chifukwa anakonda Hana, koma Yehova anatseka mimba yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 koma anapatsa Hana magawo awiri, chifukwa anakonda Hana, koma Yehova anatseka mimba yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndipo ngakhale ankakonda Hana, ankangompatsa gawo limodzi chifukwa choti Chauta sadampatse ana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ngakhale ankamukonda Hana, koma ankamupatsa gawo limodzi popeza Yehova sanamupatse ana. Onani mutuwo |