Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 2:4 - Buku Lopatulika

Maonekedwe ao aoneka ngati akavalo, nathamanga ngati akavalo a nkhondo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Maonekedwe ao aoneka ngati akavalo, nathamanga ngati akavalo a nkhondo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maonekedwe ake ali ngati a akavalo, liŵiro lake ngati la akavalo ankhondo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Maonekedwe awo ali ngati akavalo; akuthamanga ngati akavalo ankhondo.

Onani mutuwo



Yoweli 2:4
3 Mawu Ofanana  

Kumveka kwa chikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magaleta; ndi kaphatakaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magaleta;


Ndipo maonekedwe a dzombelo anafanana ndi akavalo okonzeka kukachita nkhondo; ndi pamitu pao ngati akorona onga agolide, ndi pankhope pao ngati pankhope pa anthu.


Pamenepo ziboda za akavalo zinaguguda. Ndi kutumphatumpha, kutumphatumpha kwa anthu ake eni mphamvu.