Yoweli 2:3 - Buku Lopatulika3 Moto unyambita pamaso pao, ndi m'mbuyo mwao litentha lawi la moto; kumaso kwao dziko likunga munda wa Edeni, koma m'mbuyo mwao likunga chipululu chopanda kanthu; palibenso wakuwapulumuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Moto unyambita pamaso pao, ndi m'mbuyo mwao litentha lawi la moto; kumaso kwao dziko likunga munda wa Edeni, koma m'mbuyo mwao likunga chipululu chopanda kanthu; palibenso wakuwapulumuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kutsogolo kwake moto ukupsereza, kumbuyo kwake malaŵi a moto akutentha zinthu. Iwo asanafike, dziko linali ngati munda wa Edeni, koma atachoka, lidasanduka chipululu! Palibe kanthu kotsalapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Patsogolo pawo moto ukupsereza, kumbuyo kwawo malawi amoto akutentha zinthu. Patsogolo pawo dziko lili ngati munda wa Edeni, kumbuyo kwawo kuli ngati chipululu, kulibe kanthu kotsalapo. Onani mutuwo |