Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yoweli 2:4 - Buku Lopatulika

4 Maonekedwe ao aoneka ngati akavalo, nathamanga ngati akavalo a nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Maonekedwe ao aoneka ngati akavalo, nathamanga ngati akavalo a nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Maonekedwe ake ali ngati a akavalo, liŵiro lake ngati la akavalo ankhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Maonekedwe awo ali ngati akavalo; akuthamanga ngati akavalo ankhondo.

Onani mutuwo Koperani




Yoweli 2:4
3 Mawu Ofanana  

Kumveka kwa chikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magaleta; ndi kaphatakaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magaleta;


Ndipo maonekedwe a dzombelo anafanana ndi akavalo okonzeka kukachita nkhondo; ndi pamitu pao ngati akorona onga agolide, ndi pankhope pao ngati pankhope pa anthu.


Pamenepo ziboda za akavalo zinaguguda. Ndi kutumphatumpha, kutumphatumpha kwa anthu ake eni mphamvu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa