Yoweli 2:2 - Buku Lopatulika2 tsiku la mdima, la mdima wandiweyani, tsiku la mitambo, mitambo yochindikira, ngati m'mbandakucha moyalika pamapiri; mtundu waukulu ndi wamphamvu, panalibe wotere ndi kale lonse, sipadzakhalanso wotere utapita uwu, kufikira zaka za mibadwo yambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 tsiku la mdima, la mdima wandiweyani, tsiku la mitambo, mitambo yochindikira, ngati m'mbandakucha moyalika pamapiri; mtundu waukulu ndi wamphamvu, panalibe wotere ndi kale lonse, sipadzakhalanso wotere utapita uwu, kufikira zaka za mibadwo yambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndi tsiku lamdima ndi lachisoni, tsiku lamitambo ndi la mdima wandiweyani. Gulu la ankhondo amphamvu ochuluka langoti bii ngati mdima wokuta mapiri. Gulu lotere silinaonekepo nkale lonse, ngakhale kutsogolo kuno silidzaonekanso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 tsiku la mdima ndi chisoni, tsiku la mitambo ndi la mdima wandiweyani. Ngati mʼbandakucha umene wakuta mapiri, gulu lalikulu ndi la ankhondo amphamvu likubwera, gulu limene nʼkale lomwe silinaonekepo ngakhale kutsogolo kuno silidzaonekanso. Onani mutuwo |