Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Nahumu 3:2 - Buku Lopatulika

2 Kumveka kwa chikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magaleta; ndi kaphatakaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magaleta;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Kumveka kwa chikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magaleta; ndi kaphatakaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magaleta;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Imvani kulira kwa zikoti, kukokoma kwa mikombero, likitilikiti wa akavalo ndi kulilima kwa magaleta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Kulira kwa zikwapu, mkokomo wa mikombero, kufuwula kwa akavalo ndiponso phokoso la magaleta!

Onani mutuwo Koperani




Nahumu 3:2
7 Mawu Ofanana  

Pakuti zida zonse za mwamuna wovala zida za nkhondo m'phokosomo, ndi zovala zomvimvinika m'mwazi, zidzakhala zonyeka ngati nkhuni.


Pomveka migugu ya ziboda za olimba ake, pogumukira magaleta ake, ndi pophokosera njinga zake, atate sadzacheukira ana ao chifukwa cha kulefuka kwa manja ao;


Maonekedwe ao aoneka ngati akavalo, nathamanga ngati akavalo a nkhondo.


Atumphako ngati mkokomo wa magaleta pamwamba pa mapiri, ngati kulilima kwa malawi a moto akupsereza ziputu, ngati mtundu wamphamvu wa anthu ondandalikira nkhondo.


Pamenepo ziboda za akavalo zinaguguda. Ndi kutumphatumpha, kutumphatumpha kwa anthu ake eni mphamvu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa