Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 1:1 - Buku Lopatulika

Mau a Yehova a kwa Yowele mwana wa Petuwele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mau a Yehova a kwa Yowele mwana wa Petuwele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nawu uthenga umene Chauta adapatsa Yowele, mwana wa Petuwele:

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli.

Onani mutuwo



Yoweli 1:1
5 Mawu Ofanana  

amene anamdzera mau a Yehova masiku a Yosiya mwana wake wa Amoni, mfumu ya Ayuda chaka chakhumi ndi chitatu cha ufumu wake.


anadzadi mau a Yehova kwa Ezekiele wansembe, mwana wa Buzi, m'dziko la Ababiloni kumtsinje Kebara; ndi pomwepo dzanja la Yehova lidamkhalira.


Mau a Yehova amene anadza kwa Hoseya mwana wa Beeri masiku a Uziya, Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda, ndi masiku a Yerobowamu mwana wa Yowasi mfumu ya Israele.


komatu ichi ndi chimene chinanenedwa ndi mneneri Yowele,


pakuti kale lonse chinenero sichinadze ndi chifuniro cha munthu; koma anthu a Mulungu, ogwidwa ndi Mzimu Woyera, analankhula.