Yoweli 1:2 - Buku Lopatulika2 Imvani ichi, akuluakulu inu, nimutchere khutu, inu nonse okhala m'dziko. Chachitika ichi masiku anu kodi, kapena masiku a makolo anu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Imvani ichi, akuluakulu inu, nimutchere khutu, inu nonse okhala m'dziko. Chachitika ichi masiku anu kodi, kapena masiku a makolo anu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Inu akuluakulu, mverani. Tcherani khutu, inu nonse okhala m'dziko. Kodi zoterezi zidaonekapo nthaŵi yanu kapena nthaŵi ya makolo anu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu akuluakulu, imvani izi; mvetserani, nonse amene mumakhala mʼdziko. Kodi zinthu zokhala ngati izi zinayamba zaonekapo mʼnthawi yanu, kapena mʼnthawi ya makolo anu? Onani mutuwo |