Yoweli 1:1 - Buku Lopatulika1 Mau a Yehova a kwa Yowele mwana wa Petuwele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau a Yehova a kwa Yowele mwana wa Petuwele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nawu uthenga umene Chauta adapatsa Yowele, mwana wa Petuwele: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli. Onani mutuwo |