Hoseya 14:9 - Buku Lopatulika9 Wanzeru ndani, kuti azindikire izi? Waluntha, kuti adziwe izi? Pakuti njira za Yehova zili zoongoka; ndipo olungama adzayendamo, koma olakwa adzagwamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Wanzeru ndani, kuti azindikire izi? Waluntha, kuti adziwe izi? Pakuti njira za Yehova zili zoongoka; ndipo olungama adzayendamo, koma olakwa adzagwamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amene ali wanzeru amvetse zimenezi. Amene ali womvetsa, azisunge. Pakuti njira za Chauta nzolungama, ndipo olungama amayendamo, koma ochimwa amakhumudwamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi. Ndani amene amamvetsa zinthu? Adzamvetse izi. Njira za Yehova ndi zolungama; anthu olungama amayenda mʼmenemo, koma anthu owukira amapunthwamo. Onani mutuwo |