Hoseya 14:8 - Buku Lopatulika8 Efuremu adzati, Ndili ndi chiyaninso ndi mafano? Ndayankha, ndidzampenyerera; ndili ngati mtengo wamlombwa wabiriwiri; zipatso zako zipezeka zochokera kwa Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Efuremu adzati, Ndili ndi chiyaninso ndi mafano? Ndayankha, ndidzampenyerera; ndili ngati mtengo wamlombwa wabiriwiri; zipatso zako zipezeka zochokera kwa Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kodi Aefuremu adzachita nawonso chiyani mafano? Ndine amene ndimamva pemphero lao ndi kuŵasamala. Ndili ngati mkungudza wogudira nthaŵi zonse, ndine amene ndimaŵapatsa zipatso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano? Ine ndidzamuyankha ndi kumusamalira. Ine ndili ngati mtengo wa payini wobiriwira; zipatso zako zimachokera kwa Ine.” Onani mutuwo |