Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, nafika ku Betefage, kuphiri la Azitona, pamenepo Yesu anatumiza ophunzira awiri,
Yohane 8:1 - Buku Lopatulika Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa [Koma Yesu adapita ku Phiri la Olivi. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Koma Yesu anapita ku phiri la Olivi. |
Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, nafika ku Betefage, kuphiri la Azitona, pamenepo Yesu anatumiza ophunzira awiri,
Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, paphiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ake,
Ndipo pamene anakhala Iye paphiri la Azitona, popenyana ndi Kachisi, anamfunsa Iye m'tseri Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane, ndi Andrea, kuti,
Ndipo pakuyandikira Iye tsono potsetsereka pake paphiri la Azitona, unyinji wonse wa ophunzira anayamba kukondwera ndi kuyamika Mulungu ndi mau aakulu, chifukwa cha ntchito zonse zamphamvu anaziona;