Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 8:1 - Buku Lopatulika

Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

[Koma Yesu adapita ku Phiri la Olivi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Yesu anapita ku phiri la Olivi.

Onani mutuwo



Yohane 8:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, nafika ku Betefage, kuphiri la Azitona, pamenepo Yesu anatumiza ophunzira awiri,


Ndipo pamene iwo anayandikira ku Yerusalemu, ku Betefage ndi Betaniya, paphiri la Azitona, anatuma awiri a ophunzira ake,


Ndipo pamene anakhala Iye paphiri la Azitona, popenyana ndi Kachisi, anamfunsa Iye m'tseri Petro, ndi Yakobo, ndi Yohane, ndi Andrea, kuti,


Ndipo pakuyandikira Iye tsono potsetsereka pake paphiri la Azitona, unyinji wonse wa ophunzira anayamba kukondwera ndi kuyamika Mulungu ndi mau aakulu, chifukwa cha ntchito zonse zamphamvu anaziona;


Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.