Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:5 - Buku Lopatulika

Pakuti angakhale abale ake sanakhulupirire Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti angakhale abale ake sanakhulupirira Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

(Ndiye kuti abale akewo ankatero chifukwa ngakhale iwo omwe sankamukhulupirira.)

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti ngakhale abale ake omwe sanamukhulupirire.

Onani mutuwo



Yohane 7:5
7 Mawu Ofanana  

Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka.


Koma pamene abale ake adakwera kunka kuchikondwerero, pomwepo Iyenso anakwera, si poonekera, koma monga mobisalika.


Chifukwa chake abale ake anati kwa Iye, Chokani pano, mumuke ku Yudeya, kuti ophunzira anunso akapenye ntchito zanu zimene muchita.


Pakuti palibe munthu achita kanthu mobisika, nafuna yekha kukhala poyera. Ngati muchita izi, dzionetsereni eni nokha kwa dziko lapansi.