Yohane 7:6 - Buku Lopatulika6 Chifukwa chake Yesu ananena nao, Nthawi yanga siinafike; koma nthawi yanu yakonzeka masiku onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chifukwa chake Yesu ananena nao, Nthawi yanga siinafike; koma nthawi yanu yakonzeka masiku onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Yesu adaŵauza kuti, “Nthaŵi yanga siinafikebe, koma yanu ndi nthaŵi iliyonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho Yesu anawawuza iwo kuti, “Nthawi yanga yoyenera sinafike; kwa inu nthawi ina iliyonse ndi yoyenera. Onani mutuwo |