Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:5 - Buku Lopatulika

5 Pakuti angakhale abale ake sanakhulupirire Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pakuti angakhale abale ake sanakhulupirira Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 (Ndiye kuti abale akewo ankatero chifukwa ngakhale iwo omwe sankamukhulupirira.)

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Pakuti ngakhale abale ake omwe sanamukhulupirire.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:5
7 Mawu Ofanana  

Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka.


Koma pamene abale ake adakwera kunka kuchikondwerero, pomwepo Iyenso anakwera, si poonekera, koma monga mobisalika.


Chifukwa chake abale ake anati kwa Iye, Chokani pano, mumuke ku Yudeya, kuti ophunzira anunso akapenye ntchito zanu zimene muchita.


Pakuti palibe munthu achita kanthu mobisika, nafuna yekha kukhala poyera. Ngati muchita izi, dzionetsereni eni nokha kwa dziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa