Yohane 7:7 - Buku Lopatulika7 Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthu ongokonda zapansipano sangadane nanu, koma amadana ndi Ine, chifukwa ndimapereka umboni wosonyeza kuti ntchito zao nzoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Dziko lapansi silingakudeni inu, koma limandida Ine chifukwa Ine ndimachitira umboni kuti zomwe limachita ndi zoyipa. Onani mutuwo |