Yohane 7:8 - Buku Lopatulika8 Kwerani inu kunka kuphwando; sindikwera Ine kuphwando ili tsopano apa; pakuti nthawi yanga siinakwanire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Kwerani inu kunka kuphwando; sindikwera Ine kuphwando ili tsopano apa; pakuti nthawi yanga siinakwanire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inuyo pitani kuchikondwereroko. Ine sindipitako ku chikondwerero chimenechi, chifukwa nthaŵi yanga yoyenera siinafike.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu pitani kuphwando. Ine sindipita tsopano kuphwando ili chifukwa kwa Ine nthawi yoyenera sinafike.” Onani mutuwo |