Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo m'mene adanena nao zimenezi anakhalabe mu Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo m'mene adanena nao zimenezi anakhalabe m'Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Yesu atanena zimenezo, adatsalira m'Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Atanena izi, Iye anakhalabe mu Galileya.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:9
2 Mawu Ofanana  

Koma pamene abale ake adakwera kunka kuchikondwerero, pomwepo Iyenso anakwera, si poonekera, koma monga mobisalika.


Kwerani inu kunka kuphwando; sindikwera Ine kuphwando ili tsopano apa; pakuti nthawi yanga siinakwanire.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa