Marko 3:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Achibale ake atamva zimenezi, adabwera kuti adzamtenge, chifukwa ankati, “Wachita misala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Anthu a ku banja lake atamva zimenezi, anapita kuti akamutenga, pakuti ankanena kuti, “Wazungulira mutu.” Onani mutuwo |