Marko 3:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anthu ambiri anasonkhananso, kotero kuti sanathe iwo konse kudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anthu ambiri anasonkhananso, kotero kuti sanathe iwo konse kudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pambuyo pake Yesu adapita kwao, ndipo anthu ambiri adasonkhananso, kotero kuti Iye ndi ophunzira ake analibe ndi mpata womwe wodyera chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pambuyo pake Yesu analowa mʼnyumba, ndipo gulu la anthu linasonkhananso, kotero kuti Iye pamodzi ndi ophunzira ake sanapeze mpata kuti adye. Onani mutuwo |