Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:4 - Buku Lopatulika

Ndipo anayenera kupita pakati pa Samariya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anayenera kupita pakati pa Samariya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa ulendowo ankayenera kudzera m'dziko la Samariya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.

Onani mutuwo



Yohane 4:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali, pakumuka ku Yerusalemu Iye analikupita pakati pa Samariya ndi Galileya.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Kuli bwanji kuti munalikundifunafuna Ine? Simunadziwa kodi kuti kundiyenera Ine ndikhale m'zake za Atate wanga?


Ndipo tsiku la mikate yopanda chotupitsa linafika, limene inayenera kuphedwa nsembe ya Paska.