Yohane 4:5 - Buku Lopatulika5 Chifukwa chake anadza kumzinda wa Samariya, dzina lake Sikari, pafupi pa kadziko kamene Yakobo adapatsa mwana wake Yosefe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chifukwa chake anadza kumudzi wa Samariya, dzina lake Sikari, pafupi pa kadziko kamene Yakobo adapatsa mwana wake Yosefe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono adafika ku mudzi wina wa ku Samariya, dzina lake Sikari, pafupi ndi kadziko kamene Yakobe adaapatsa Yosefe, mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anafika mʼmudzi wa Asamariya wotchedwa Sukari, pafupi ndi malo amene Yakobo anapatsa mwana wake Yosefe. Onani mutuwo |