Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo anayenera kupita pakati pa Samariya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo anayenera kupita pakati pa Samariya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Pa ulendowo ankayenera kudzera m'dziko la Samariya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali, pakumuka ku Yerusalemu Iye analikupita pakati pa Samariya ndi Galileya.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Kuli bwanji kuti munalikundifunafuna Ine? Simunadziwa kodi kuti kundiyenera Ine ndikhale m'zake za Atate wanga?


Ndipo tsiku la mikate yopanda chotupitsa linafika, limene inayenera kuphedwa nsembe ya Paska.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa