Yohane 4:6 - Buku Lopatulika6 ndipo pamenepo panali chitsime cha Yakobo. Ndipo Yesu, popeza analema ndi ulendo wake, motero anakhala pachitsime. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo pamenepo panali chitsime cha Yakobo. Ndipo Yesu, popeza analema ndi ulendo wake, motero anakhala ndi ulendo wake, motero anakhala pachitsime. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kumeneko kunali chitsime cha Yakobe. Yesu adakhala pansi pambali pa chitsimecho, chifukwa anali atatopa ndi ulendo. Nthaŵi inali ngati 12 koloko masana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Chitsime cha Yakobo chinali pamenepo ndipo Yesu atatopa ndi ulendo anakhala pansi pambali pa chitsimecho. Nthawi inali pafupifupi ora lachisanu ndi chimodzi masana. Onani mutuwo |