Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:2 - Buku Lopatulika

(angakhale Yesu sanabatize yekha koma ophunzira ake),

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

(angakhale Yesu sanabatize yekha koma ophunzira ake),

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

(Komabe amene ankabatiza si Yesuyo, koma ophunzira ake).

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(ngakhale kuti Yesuyo sankabatiza, koma ophunzira ake).

Onani mutuwo



Yohane 4:2
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Zitapita izi anadza Yesu ndi ophunzira ake kudziko la Yudeya; ndipo pamenepo anatsotsa nao pamodzi, nabatiza.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.


Ndipo analamulira iwo abatizidwe m'dzina la Yesu Khristu. Pamenepo anampempha iye atsotse masiku.