Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 3:22 - Buku Lopatulika

22 Zitapita izi anadza Yesu ndi ophunzira ake kudziko la Yudeya; ndipo pamenepo anatsotsa nao pamodzi, nabatiza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Zitapita izi anadza Yesu ndi ophunzira ake kudziko la Yudeya; ndipo pamenepo anatsotsa nao pamodzi, nabatiza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Pambuyo pake Yesu ndi ophunzira ake adapita ku dera la Yudeya. Adakhala nawo kumeneko kanthaŵi, ndipo ankabatiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Zitatha izi, Yesu ndi ophunzira ake anapita mʼmadera a ku midzi ya ku Yudeya, kumene Iye anakhala kanthawi akubatiza.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 3:22
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Paska wa Ayuda unayandikira, ndipo Yesu anakwera kunka ku Yerusalemu.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Ndipo Yohane analinkubatiza mu Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.


Chifukwa chake abale ake anati kwa Iye, Chokani pano, mumuke ku Yudeya, kuti ophunzira anunso akapenye ntchito zanu zimene muchita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa