Yohane 3:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Yohane analinkubatiza mu Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Yohane analinkubatiza m'Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Yohane nayenso ankabatiza ku Ainoni pafupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri. Anthu ankafikako, iye nkumaŵabatiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo Yohane amabatizanso ku Ainoni kufupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri ndipo anthu amabwererabwererabe kudzabatizidwa. Onani mutuwo |