Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 3:24 - Buku Lopatulika

24 Pakuti Yohane sanaikidwe m'ndende.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Pakuti Yohane sanaikidwe m'ndende.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Pamenepo nkuti Yohane asanaponyedwe m'ndende.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 (Apa nʼkuti Yohane asanatsekeredwe mʼndende).

Onani mutuwo Koperani




Yohane 3:24
6 Mawu Ofanana  

Pakuti Herode adamgwira Yohane, nammanga, namuika m'nyumba yandende chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa mbale wake Filipo.


Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya;


Pakuti Herode, mwini yekha, adatuma anthu namgwira Yohane, nammanga m'nyumba yandende, chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa Filipo mbale wake; chifukwa adamkwatira iye.


Ndipo Yohane analinkubatiza mu Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa