Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 12:4 - Buku Lopatulika

Koma Yudasi Iskariote, mmodzi wa ophunzira ake, amene adzampereka Iye, ananena,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yudasi Iskariote, mmodzi wa ophunzira ake, amene adzampereka Iye, ananena,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Yudasi Iskariote, mmodzi mwa ophunzira a Yesu, amene analikudzampereka kwa adani ake, adati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma mmodzi wa ophunzira ake, Yudasi Isikarioti, amene pambuyo pake adzamupereka anati,

Onani mutuwo



Yohane 12:4
10 Mawu Ofanana  

Ndiponso ndinapenyera mavuto onse ndi ntchito zonse zompindulira bwino, kuti chifukwa cha zimenezi anansi ake achitira munthu nsanje. Ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Simoni Mkanani, ndi Yudasi Iskariote amenenso anampereka Iye.


Pomwepo mmodzi wa khumi ndi awiriwo, dzina lake Yudasi Iskariote, anamuka kwa ansembe aakulu,


ndi Yudasi mwana wa Yakobo, ndi Yudasi Iskariote, amene anali wompereka Iye.


Nanga mafuta onunkhira awa sanagulitsidwe chifukwa ninji ndi marupiya atheka mazana atatu, ndi kupatsidwa kwa osauka?


Ndipo pokhala pamgonero, mdierekezi adatha kuika mu mtima wake wa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote, kuti akampereke Iye,


Ndipo Yesu anayankha, Ndi iyeyu, amene Ine ndidzamsunsira nthongo ndi kumpatsa. Pamenepo, m'mene anasunsa nthongo anaitenga naipatsa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote.