Yohane 12:5 - Buku Lopatulika5 Nanga mafuta onunkhira awa sanagulitsidwe chifukwa ninji ndi marupiya atheka mazana atatu, ndi kupatsidwa kwa osauka? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nanga mafuta onunkhira awa sanagulitsidwa chifukwa ninji ndi marupiya atheka mazana atatu, ndi kupatsidwa kwa osauka? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Kodi bwanji mafuta ameneŵa sadaŵagulitse ndalama mazana atatu kenaka ndalamazo nkukapatsa anthu osauka?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Nʼchifukwa chiyani mafuta awa sanagulitsidwe ndipo ndalama zake nʼkuzipereka kwa osauka?” Mafutawo anali a mtengo wa malipiro a chaka chimodzi. Onani mutuwo |