Yohane 12:6 - Buku Lopatulika6 Koma ananena ichi si chifukwa analikusamalira osauka, koma chifukwa anali mbala, ndipo pokhala nalo thumba, amaba zoikidwamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ananena ichi si chifukwa analikusamalira osauka, koma chifukwa anali mbala, ndipo pokhala nalo thumba, amaba zoikidwamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adaatero osati chifukwa chodera nkhaŵa osaukawo, koma chifukwa anali mbala. Iye ankasunga thumba la ndalama, nkumabamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye sananene izi chifukwa cha kuganizira osauka koma chifukwa anali mbava; ngati wosunga thumba la ndalama, amabamo zomwe ankayikamo. Onani mutuwo |