Yohane 12:7 - Buku Lopatulika7 Pamenepo Yesu anati, Mleke iye, pakuti anachisungira ichi tsiku la kuikidwa kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamenepo Yesu anati, Mleke iye, pakuti anachisungira ichi tsiku la kuikidwa kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Yesu adati, “Mlekeni, mafutaŵa aŵasungire tsiku lodzaika maliro anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yesu anayankha kuti, “Mulekeni. Mafutawa anayenera kusungidwa mpaka tsiku loyika maliro anga. Onani mutuwo |