Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 12:7 - Buku Lopatulika

7 Pamenepo Yesu anati, Mleke iye, pakuti anachisungira ichi tsiku la kuikidwa kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pamenepo Yesu anati, Mleke iye, pakuti anachisungira ichi tsiku la kuikidwa kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Yesu adati, “Mlekeni, mafutaŵa aŵasungire tsiku lodzaika maliro anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Yesu anayankha kuti, “Mulekeni. Mafutawa anayenera kusungidwa mpaka tsiku loyika maliro anga.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 12:7
9 Mawu Ofanana  

Popeza adzaima padzanja lamanja la waumphawi, kumpulumutsa kwa iwo akuweruza koipa moyo wake.


Ndipo Yehova anati kwa Satana, Yehova akudzudzula, Satana iwe; inde Yehova amene anasankha Yerusalemu akudzudzula; uyu sindiye muuni wofumulidwa kumoto?


Koma Yesu podziwa, anati kwa iwo, Mumvutiranji mkaziyu? Popeza andichitira Ine ntchito yabwino.


Pakuti mkaziyo, m'mene anathira mafuta awa pathupi panga, wandichitiratu ichi pa kuikidwa kwanga.


Koma Yesu anati, Mlekeni, mumvutiranji? Wandichitira Ine ntchito yabwino.


Ndipo taonani, munthu dzina lake Yosefe, ndiye mkulu wa milandu, munthu wabwino ndi wolungama


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa