Yohane 12:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti osauka muli nao pamodzi ndi inu nthawi zonse; koma simuli ndi Ine nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti osauka muli nao pamodzi ndi Ine nthawi zonse; koma simuli ndi Inu nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pajatu osauka muli nawo nthaŵi zonse, koma Ine simudzakhala nane nthaŵi zonse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu mudzakhala ndi osauka nthawi zonse, koma simudzakhala nane nthawi zonse.” Onani mutuwo |