Mateyu 26:14 - Buku Lopatulika14 Pomwepo mmodzi wa khumi ndi awiriwo, dzina lake Yudasi Iskariote, anamuka kwa ansembe aakulu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pomwepo mmodzi wa khumi ndi awiriwo, dzina lake Yudasi Iskariote, anamuka kwa ansembe aakulu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pambuyo pake Yudasi Iskariote, mmodzi mwa ophunzira khumi ndi aŵiri aja, adapita kwa akulu a ansembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pamenepo mmodzi wa khumi ndi awiriwo wotchedwa Yudasi Isikarioti anapita kwa akulu a ansembe Onani mutuwo |