Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:8 - Buku Lopatulika

Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye sindiye kuunikaku, koma anatumidwa kukachita umboni wa kuunikaku.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Sikuti iyeyo ndiye anali kuŵalako ai, koma adangobwera kudzachitira umboni kuŵalako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iyeyu sanali kuwunika; koma anabwera ngati mboni ya kuwunika.

Onani mutuwo



Yohane 1:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anavomera, wosakana; nalola kuti, Sindine Khristu.


Uku ndiko kuunika kwenikweni, kumene kuunikira anthu onse akulowa m'dziko lapansi.


Inu nokha mundichitira umboni, kuti ndinati, Sindine Khristu, koma kuti ndili wotumidwa m'tsogolo mwake mwa Iye.


Ndipo anati Paulo, Yohane anabatiza ndi ubatizo wa kutembenuka mtima, nati kwa anthu, kuti amkhulupirire Iye amene adzadza pambuyo pake, ndiye Yesu.