Yohane 3:28 - Buku Lopatulika28 Inu nokha mundichitira umboni, kuti ndinati, Sindine Khristu, koma kuti ndili wotumidwa m'tsogolo mwake mwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Inu nokha mundichitira umboni, kuti ndinati, Sindine Khristu, koma kuti ndili wotumidwa m'tsogolo mwake mwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Inu nomwe ndinu mboni zanga kuti ndidati, ‘Sindine Mpulumutsi wolonjezedwa uja, koma ndine wotumidwa patsogolo pake.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Inuyo ndinu mboni zanga kuti ine ndinati, ‘Ine sindine Khristu koma ndatumidwa patsogolo pa Iye.’ Onani mutuwo |