Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:68 - Buku Lopatulika

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso kambale kamodzi kagolide ka magaramu 110, kodzaza ndi lubani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mbale imodzi yagolide yolemera magalamu 110, yodzaza ndi lubani;

Onani mutuwo



Numeri 7:68
3 Mawu Ofanana  

Pemphero langa liikike ngati chofukiza pamaso panu; kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo.


chipande chimodzi chagolide cha masekeli khumi, chodzala ndi chofukiza;


ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;