Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:16 - Buku Lopatulika

tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaperekanso tonde mmodzi woperekera nsembe yopepesera machimo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mbuzi yayimuna imodzi, nsembe ya machimo;

Onani mutuwo



Numeri 7:16
3 Mawu Ofanana  

akamdziwitsa kuchimwa kwake adachimwako, azidza nacho chopereka chake, ndicho tonde wopanda chilema;


Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yauchimo ndi chala chake, nauike pa nyanga za guwa la nsembe yopsereza, ndi kuthira mwazi wake patsinde pa guwa la nsembe yopsereza.


ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwanawankhosa mmodzi wa chaka chimodzi, zikhale nsembe yopsereza;