Levitiko 4:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yauchimo ndi chala chake, nauike pa nyanga za guwa la nsembe yopsereza, ndi kuthira mwazi wake patsinde pa guwa la nsembe yopsereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo wansembe atengeko mwazi wa nsembe yauchimo ndi chala chake, nauike pa nyanga za guwa la nsembe yopsereza, ndi kuthira mwazi wake patsinde pa guwa la nsembe yopsereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Wansembe atengeko magazi a tondeyo ndi chala chake, aŵapake pa nyanga za guwa la nsembe zopsereza, ndi kuthira magazi otsalowo patsinde pa guwa lomwelo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pambuyo pake wansembe atengeko magazi a chopereka chopepesera tchimocho ndi chala chake, ndipo awapake pa nyanga za guwa lansembe zopsereza. Athire magazi otsalawo pa tsinde la guwalo. Onani mutuwo |