Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 7:16 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 mbuzi yayimuna imodzi, nsembe ya machimo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

16 tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Adaperekanso tonde mmodzi woperekera nsembe yopepesera machimo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:16
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati wauzidwa za tchimo limene wachita, iye abwere ndi mbuzi yayimuna yopanda chilema kuti ikhale chopereka chake.


Pambuyo pake wansembe atengeko magazi a chopereka chopepesera tchimocho ndi chala chake, ndipo awapake pa nyanga za guwa lansembe zopsereza. Athire magazi otsalawo pa tsinde la guwalo.


mwana wangʼombe wamwamuna mmodzi, nkhosa yayimuna imodzi ndi mwana wankhosa wamwamuna mmodzi wa chaka chimodzi, za nsembe yopsereza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa