Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 6:6 - Buku Lopatulika

Masiku onse akudzipatulira kwa Yehova asayandikize mtembo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Masiku onse akudzipatulira kwa Yehova asayandikize mtembo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Masiku onse pamene munthuyo wadzipereka kwa Chauta, asayandikire mtembo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa nthawi yonse imene munthuyo wadzipatula yekha kwa Yehova asayandikire mtembo.

Onani mutuwo



Numeri 6:6
10 Mawu Ofanana  

Musamadzicheka matupi anu chifukwa cha akufa, kapena kutema mphini; Ine ndine Yehova.


Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake.


Asatuluke m'malo opatulika, kapena kuipsa malo opatulika a Mulungu wake; popeza korona wa mafuta odzoza wa Mulungu wake ali pa iye; Ine ndine Yehova.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.