Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 21:11 - Buku Lopatulika

11 Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Asakaloŵe kumene kuli munthu wakufa aliyense ndi kudziipitsa, ngakhale mtembo wa bambo wake kapena wa mai wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Asalowe mʼnyumba mmene muli munthu wakufa ngakhale womwalirayo ndi amayi ake kapena abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 21:11
11 Mawu Ofanana  

Musamadzicheka matupi anu chifukwa cha akufa, kapena kutema mphini; Ine ndine Yehova.


Iye wakukhudza mtembo wa munthu aliyense adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri;


Chilamulo ndi ichi: Munthu akafa m'hema, yense wakulowa m'hemamo, ndi yense wakukhala m'hemamo, adzakhala wodetsedwa masiku asanu ndi awiri.


Asadzidetse ndi atate wake, kapena mai wake, mbale wake, kapena mlongo wake, akafa iwowa; popeza chowindira Mulungu wake chili pamutu pake.


Munthu akadza kwa Ine, wosada atate wake ndi amake, ndi mkazi wake, ndi ana, ndi abale, ndi alongo ake, inde ndi moyo wake womwe wa iye mwini, sangathe kukhala wophunzira wanga.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.


amene anati za atate wake ndi amai wake, sindinamuone; Sanazindikire abale ake, sanadziwe ana ake omwe; popeza anasamalira mau anu, nasunga chipangano chanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa