Levitiko 21:11 - Buku Lopatulika11 Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Asakaloŵe kumene kuli munthu wakufa aliyense ndi kudziipitsa, ngakhale mtembo wa bambo wake kapena wa mai wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Asalowe mʼnyumba mmene muli munthu wakufa ngakhale womwalirayo ndi amayi ake kapena abambo ake. Onani mutuwo |