Numeri 6:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pa nthawi yonse imene munthuyo wadzipatula yekha kwa Yehova asayandikire mtembo. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 Masiku onse akudzipatulira kwa Yehova asayandikize mtembo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Masiku onse akudzipatulira kwa Yehova asayandikize mtembo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Masiku onse pamene munthuyo wadzipereka kwa Chauta, asayandikire mtembo. Onani mutuwo |