Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:44 - Buku Lopatulika

owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chiŵerengero chao chidakwanira 3,200 potsata mabanja ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 3,200.

Onani mutuwo



Numeri 4:44
7 Mawu Ofanana  

Ndipo owerengedwa ao, powerenga amuna onse, kuyambira a mwezi umodzi ndi mphambu, ndiwo zikwi zisanu ndi chimodzi kudza mazana awiri.


kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako,


Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Merari, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.


Sichinakugwerani inu chiyeso koma cha umunthu; koma Mulungu ali wokhulupirika, amene sadzalola inu kuyesedwa koposa kumene mukhoza; koma pamodzi ndi chiyeso adzaikanso populumukirapo, kuti mudzakhoze kupirirako.


Nsapato zako zikhale za chitsulo ndi mkuwa; ndipo monga masiku ako momwemo mphamvu yako.