Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:8 - Buku Lopatulika

Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anatero makolo anu, muja ndinawatumiza achoke ku Kadesi-Baranea kukaona dziko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Makolo anu adachita zotero, pamene ndidaŵatuma kuchokera ku Kadesi-Baranea, kuti akaone dziko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi ndi zimene makolo anu anachita pamene ndinawatuma kuchokera ku Kadesi kukaona dzikolo.

Onani mutuwo



Numeri 32:8
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ana onse a Israele anadandaulira Mose ndi Aroni; ndi khamu lonse linanena nao, Mwenzi tikadafa m'dziko la Ejipito; kapena mwenzi tikadafa m'chipululu muno!


ndi malire anu adzapinda kuchokera kumwera kunka pokwera Akarabimu, ndi kupitirira ku Zini; ndi kutuluka kwake adzachokera kumwera ku Kadesi-Baranea, nadzatuluka kunka ku Hazara-Adara, ndi kupita kunka ku Azimoni;


Ulendo wake wochokera ku Horebu wofikira ku Kadesi-Baranea, wodzera njira ya phiri la Seiri, ndiwo wa masiku khumi ndi limodzi.