Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:34 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Gadi anamanga Diboni, ndi Ataroti, ndi Aroere;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Gadi anamanga Diboni, ndi Ataroti, ndi Aroere;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a Gadi adamanga mizinda ya Diboni, Ataroti, Aroere,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Agadi anamanga Diboni, Ataroti, Aroeri,

Onani mutuwo



Numeri 32:34
9 Mawu Ofanana  

ndi Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, mwana wa Yowele, wokhala ku Aroere, ndi kufikira ku Nebo ndi Baala-Meoni;


Mizinda ya Aroere yasiyidwa; idzakhala ya zoweta zogona pansi, opanda woziopsa.


atachoka ku Bamoti ku chigwa chili m'dziko la Mowabu, ku mutu wa Pisiga, popenyana ndi chipululu.


Tinawagwetsa; Hesiboni waonongeka kufikira ku Diboni, ndipo tinawapululutsa kufikira ku Nofa. Ndiwo wakufikira ku Medeba.


Ataroti, ndi Diboni, ndi Yazere, ndi Nimira, ndi Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Sibima, ndi Nebo, ndi Beoni,


Ataroti-Sofani, Yazere, ndi Yogobeha;


Kuyambira ku Aroere, ndiko kumphepete kwa mtsinje wa Arinoni, ndi kumudzi wokhala kumtsinje kufikira ku Giliyadi, kunalibe mzinda wakutitalikira malinga ake; Yehova Mulungu wathu anapereka yonse pamaso pathu.


nawakantha kuyambira ku Aroere mpaka ufika ku Miniti, ndiyo mizinda makumi awiri, ndi ku Abele-Keranimu, makanthidwe aakulu ndithu. Motero ana a Amoni anagonjetsedwa pamaso pa ana a Israele.