1 Mbiri 5:8 - Buku Lopatulika8 ndi Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, mwana wa Yowele, wokhala ku Aroere, ndi kufikira ku Nebo ndi Baala-Meoni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndi Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, mwana wa Yowele, wokhala ku Aroere, ndi kufikira ku Nebo ndi Baala-Meoni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 ndiponso Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, wa banja la Yowele. Onsewo ankakhala ku Aroere mpaka kukafika ku Nebo ndi ku Baala-Meoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 ndiponso Bela mwana wa Azazi, mwana wa Sema, mwana wa Yoweli. Iwo ankakhala ku Aroeri mpaka ku Nebo ndi Baala-Meoni. Onani mutuwo |