Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:23 - Buku Lopatulika

Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa chihema kumadzulo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa Kachisi kumadzulo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mabanja a Geresoni ankamanga zithando zao kumbuyo kwa chihema cha Mulungu mbali yakuzambwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mabanja a Ageresoni azimanga misasa yawo kumadzulo, kumbuyo kwa Chihema.

Onani mutuwo



Numeri 3:23
4 Mawu Ofanana  

Koma Alevi amange mahema ao pozungulira pa chihema cha mboni, kuti mkwiyo ungagwere khamu la ana a Israele; ndipo Alevi azidikira chihema cha mboni.


Pamenepo khamu la Alevi azimuka nacho chihema chokomanako, pakati pa makamu; monga amamanga mahema ao, momwemo azimuka ulendo wao, munthu yense pamalo pake, monga mwa mbendera zao.


Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.


Ndipo kalonga wa nyumba ya makolo a Ageresoni ndiye Eliyasafu mwana wa Laele.